Masauko Chipembere
From Wikipedia
Henry Masauko Blasius Chipembere (5 August 1930 - 24 September 1974) anali mmodzi wa anthu amene anafuna kuti anthu a ku Malawi adzilamulire okha komanso anali mphunzitso wa mbiri ku Universty ya UCLA.
[edit] Ntchito
Ngati mmodzi wa anthu amene ankakhulupilira kuti anthu a ku Malawi adzilamulire paokha, a Chipembere anali mmodzi wa anthu a chipani cha ]]Nyasaland African Congress]], wachiwiri wa woyang'anira boma la Domasi komanso . Dziko la Nyasaland litalandira ufulu wodzilamulira iwo anali msungichuma wa chipani cha Malawi Congress Party ndi nduna yoyang'anira za maboma aang'ono komanso nduna ya maphunziro.
[edit] Source
- Henry Masauko Blasius Chipembere on the African People DatabaseTemplate:Malawi-politician-stub